top of page

Mau a masiku onse

Buku iri lidzakutsogolerani m’Baibulo ndi zowerenga za tsiku lirilonse ndi mau ofotokozera ndime za m’Baibulo.

​

Tengani buku APA.

Mupangiridwa kulemba mbali zonse ziwiri.

Katekisma wa Heidelberg

Katekisma wa Heidelberg itiphunzitsa mfundo zikulu-zikulu za m'Baibulo.

Tengani Katekisma wa Heidelberg (Chichewa-Cingerezi) APA.

Zitanthauzo za mau ogwiritsidwa nchito m'Cikristu

Tengani mau APA.

  • YouTube

Kulembanso zinthu ndi colinga copangirapo ndalama sikuloledwa.

©2024 Stephanos Zambia Trust

Mfundo yosunga zisinsi

bottom of page